Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 26:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Patapita nthawi, Abimeleki anafika kwa iye kuchokera ku Gerari. Anafika limodzi ndi Ahuzati bwenzi lake lapamtima, komanso Fikolo mkulu wa asilikali ake.+

  • 1 Mafumu 4:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Azariya mwana wa Natani+ anali mkulu wa nduna, ndipo Zabudu mwana wa Natani anali wansembe, bwenzi+ la mfumu.

  • Miyambo 17:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Bwenzi lenileni limakukonda nthawi zonse,+ ndipo bwenzilo ndi m’bale amene anabadwira kuti akuthandize pakagwa mavuto.+

  • Miyambo 18:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Pali mabwenzi amene amafuna kuthyolana,+ koma pali bwenzi limene limamatirira kuposa m’bale wako.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena