Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 15:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Pakati pa Asa ndi Basa mfumu ya Isiraeli pankachitika nkhondo masiku awo onse.+

  • 1 Mafumu 16:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Tsopano ine ndidzaseseratu Basa ndi nyumba yake, ndipo ndidzachititsa nyumba yake kukhala ngati nyumba ya Yerobowamu mwana wa Nebati.+

  • 1 Mafumu 16:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Choncho Zimiri anafafaniza nyumba yonse ya Basa,+ malinga ndi mawu a Yehova+ otsutsana ndi Basa amene analankhula kudzera mwa Yehu mneneri.+

  • 2 Mbiri 16:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “Pali pangano pakati pa ine ndi iwe, ndi pakati pa bambo anga ndi bambo ako. Taona, ndakutumizira siliva ndi golide. Pita ukaphwanye pangano lako ndi Basa+ mfumu ya Isiraeli kuti achoke kwa ine.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena