Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 19:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Eliteke, Gebetoni,+ Baalati,+

  • Yoswa 21:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Kuchokera m’fuko la Dani, anawapatsa Eliteke ndi malo ake odyetserako ziweto, Gebetoni+ ndi malo ake odyetserako ziweto,

  • 1 Mafumu 16:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 M’chaka cha 27 cha Asa mfumu ya Yuda, Zimiri anakhala mfumu ku Tiriza kwa masiku 7.+ Pa nthawiyo anthu anali atamanga msasa pafupi ndi mzinda wa Gebetoni,+ umene unali wa Afilisiti, kuti authire nkhondo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena