Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 6:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pamatabwa a mkungudza a mkati mwa nyumbayo anajambulapo mochita kugoba zokongoletsera zooneka ngati zipanda+ ndi nkhata zamaluwa.+ Mkati monse munali matabwa a mkungudza ndipo simunkaoneka mwala uliwonse.

  • 2 Mafumu 4:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Choncho wina anapita kutchire kukathyola masamba,+ ndipo anapezako kamtengo koyanga, n’kuthyolapo mphonda zakutchire kudzaza pachovala chake. Atatero anabwera nazo n’kuziduladula. Kenako anazithira mumphika uja, koma iwo sankazidziwa bwinobwino.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena