Genesis 44:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Zitatero, iwo anang’amba zovala zawo.+ Kenako aliyense anakwezanso thumba lake pabulu wake n’kubwerera kumzinda kuja. 2 Samueli 1:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Davide atamva zimenezi anagwira zovala zake ndi kuzing’amba.+ Nawonso amuna onse amene anali ndi Davide anang’amba zovala zawo. 2 Mbiri 34:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Mfumuyo itangomva mawu a chilamulowo, nthawi yomweyo inang’amba zovala zake.+ Yeremiya 36:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Iwo sanachite mantha+ ndipo mfumu ndi atumiki ake onse amene anali kumvetsera mawu amenewa sanang’ambe zovala zawo.+ Yoweli 2:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Ng’ambani mitima yanu+ osati zovala zanu+ ndipo bwererani kwa Yehova Mulungu wanu pakuti iye ndi wachisomo, wachifundo,+ wosakwiya msanga+ ndiponso wodzaza ndi kukoma mtima kosatha.+ Ndithu, iye adzakumverani chisoni chifukwa cha tsokalo.+
13 Zitatero, iwo anang’amba zovala zawo.+ Kenako aliyense anakwezanso thumba lake pabulu wake n’kubwerera kumzinda kuja.
11 Davide atamva zimenezi anagwira zovala zake ndi kuzing’amba.+ Nawonso amuna onse amene anali ndi Davide anang’amba zovala zawo.
24 Iwo sanachite mantha+ ndipo mfumu ndi atumiki ake onse amene anali kumvetsera mawu amenewa sanang’ambe zovala zawo.+
13 Ng’ambani mitima yanu+ osati zovala zanu+ ndipo bwererani kwa Yehova Mulungu wanu pakuti iye ndi wachisomo, wachifundo,+ wosakwiya msanga+ ndiponso wodzaza ndi kukoma mtima kosatha.+ Ndithu, iye adzakumverani chisoni chifukwa cha tsokalo.+