Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 9:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Yezebeli adzadyedwa ndi agalu+ m’munda wa ku Yezereeli, ndipo palibe amene adzamuike m’manda.’” Mtumikiyo atamaliza kunena zimenezi, anatsegula chitseko n’kuthawa.+

  • Yesaya 14:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Sudzakhalira nawo limodzi m’manda, chifukwa unawononga dziko lako lomwe, ndipo unapha anthu ako omwe. Mayina a ana a anthu ochita zoipa sadzatchulidwanso mpaka kalekale.+

  • Yeremiya 22:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Adzaikidwa m’manda ngati mmene amaikira bulu wamphongo.+ Adzamukoka kudutsa naye pazipata za Yerusalemu ndi kukamutaya kunja.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena