Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 18:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Pansi, mizu yake idzauma.+

      Pamwamba, nthambi yake idzafota.

  • Salimo 21:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mudzawononga ana awo kuwachotsa padziko lapansi,+

      Ndipo ana awo mudzawachotsa pakati pa ana a anthu.+

  • Salimo 37:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Pakuti Yehova amakonda chilungamo,+

      Ndipo sadzasiya anthu ake okhulupirika.+

      ע [ʽAʹyin]

      Adzawateteza mpaka kalekale.+

      Koma ana a anthu oipa adzaphedwa.+

  • Salimo 109:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mbadwa zake ziphedwe ndi kuchotsedwa m’dziko.+

      Dzina lawo lifafanizidwe mu m’badwo wotsatira.+

  • Salimo 137:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iwe mwana wamkazi wa Babulo, amene udzafunkhidwa,+

      Wodala ndi amene adzakubwezera+

      Zimene iwe watichitira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena