Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 2:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Tsopano imva izi, masiku adzafika pamene ndidzadula dzanja lako ndi la nyumba ya kholo lako, moti m’nyumba yako simudzakhala munthu wokalamba.+

  • 2 Mafumu 10:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kuwonjezera apo, Yehu anapitiriza kupha onse a m’nyumba ya Ahabu amene anatsala ku Yezereeli, amuna ake onse olemekezeka,+ anzake, ndi ansembe ake,+ mpaka onse anatha.+

  • Salimo 37:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Pakuti Yehova amakonda chilungamo,+

      Ndipo sadzasiya anthu ake okhulupirika.+

      ע [ʽAʹyin]

      Adzawateteza mpaka kalekale.+

      Koma ana a anthu oipa adzaphedwa.+

  • Yeremiya 22:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Yehova wanena kuti, ‘Lembani kuti munthu uyu alibe ana,+ munthu wamphamvu amene zinthu sizidzamuyendera bwino m’masiku a moyo wake. Pakuti mwa ana ake onse, palibe ndi mmodzi yemwe amene zinthu zidzamuyendera bwino.+ Palibe ngakhale mmodzi amene adzakhala pampando wachifumu wa Davide+ ndi kulamulira mu Yuda.’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena