Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 18:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Tsopano tumizani uthenga ndipo musonkhanitse Aisiraeli onse kwa ine paphiri la Karimeli.+ Musonkhanitsenso aneneri 450 a Baala+ ndi aneneri 400 a mzati wopatulika,+ amene amadya patebulo la Yezebeli.”+

  • 1 Mafumu 22:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Choncho mfumu ya Isiraeli inasonkhanitsa aneneri pamodzi.+ Analipo amuna pafupifupi 400, ndipo inawafunsa kuti: “Kodi ndipite kukamenyana ndi Ramoti-giliyadi, kapena ndisapite?” Iwo anayankha kuti: “Pitani,+ ndipo Yehova akapereka mzindawo m’manja mwanu mfumu.”

  • 2 Mafumu 23:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Chotero iye anapha ansembe onse+ a m’malo okwezeka n’kuwapereka nsembe pamaguwa ansembe kumeneko. Kenako anawotcha mafupa a anthu pamaguwa ansembewo.+ Atatero anabwerera ku Yerusalemu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena