Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 19:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Alameleki, Amadi, ndi Misali.+ Analowera chakumadzulo ku Karimeli+ ndi ku Sihori-libanati.

  • 2 Mafumu 2:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Elisa anapitiriza ulendo wake mpaka kuphiri la Karimeli.+ Atachoka kumeneko anabwerera n’kupita ku Samariya.

  • Yeremiya 46:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 “‘Pali ine Mulungu wamoyo, Nebukadirezara adzabwera ndi kuonekera ngati phiri la Tabori+ pakati pa mapiri ena, ndiponso ngati phiri la Karimeli+ m’mphepete mwa nyanja,’ yatero Mfumu, imene dzina lake ndi Yehova wa makamu.+

  • Amosi 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Iye anati:

      “Yehova adzabangula ngati mkango mu Ziyoni,+ ndipo adzafuula mu Yerusalemu.+ Malo amene abusa amadyetserako ziweto adzalira, ndipo pansonga ya phiri la Karimeli padzauma.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena