Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 13:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Zimenezi zinachimwitsa nyumba yonse ya Yerobowamu,+ ndipo inayenera kuwonongedwa ndi kufafanizidwa padziko lapansi.+

  • Salimo 9:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mwadzudzula anthu a mitundu ina,+ mwawononga oipa.+

      Dzina lawo mwalifafaniza mpaka kalekale, mwalifafaniza mpaka muyaya.+

  • Salimo 37:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Pakuti Yehova amakonda chilungamo,+

      Ndipo sadzasiya anthu ake okhulupirika.+

      ע [ʽAʹyin]

      Adzawateteza mpaka kalekale.+

      Koma ana a anthu oipa adzaphedwa.+

  • Mateyu 25:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Ndipo iwowa adzachoka kupita ku chiwonongeko chotheratu,+ koma olungama ku moyo wosatha.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena