Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 11:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Koma Yehoseba+ mwana wamkazi wa Mfumu Yehoramu, mlongo wake wa Ahaziya, anaba Yehoasi+ mwana wamwamuna wa Ahaziya, pakati pa ana aamuna a mfumu amene anayenera kuphedwa. Anatenga Yehoasi pamodzi ndi mlezi wake n’kukamubisa+ m’chipinda chamkati chogona kuti Ataliya asamuone, moti sanaphedwe.

  • 2 Mbiri 23:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kenako anatulutsa mwana wa mfumu uja.+ Atatero anamuveka chisoti chachifumu+ n’kuika mpukutu wa Chilamulo cha Mulungu pamutu pake.+ Chotero anamulonga ufumu, ndipo Yehoyada ndi ana ake anamudzoza+ n’kuyamba kunena kuti: “Mfumu ikhale ndi moyo wautali!”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena