Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 7:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Nyumba yako ndi ufumu wako zidzakhazikika pamaso pako mpaka kalekale. Mpando wako wachifumu udzakhazikika mpaka kalekale.”’”+

  • 1 Mbiri 29:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Chotero, Solomo anayamba kukhala pampando wachifumu wa Yehova+ monga mfumu m’malo mwa Davide bambo wake, ndipo ankalamulira bwino.+ Aisiraeli onse anali kumumvera.

  • Yeremiya 17:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 pazipata za mzindawu padzalowa mafumu ndi akalonga+ okhala pampando wachifumu wa Davide.+ Mafumuwo pamodzi ndi akalonga awo adzalowa atakwera magaleta ndi mahatchi. Adzalowa pamodzi ndi anthu a mu Yuda komanso anthu okhala mu Yerusalemu ndipo mumzindawu mudzakhala anthu mpaka kalekale.

  • Yeremiya 22:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Mukatsatiradi mawu amenewa, pazipata za nyumba iyi padzalowa mafumu okhala pampando wachifumu wa Davide.+ Mfumu iliyonse idzalowa pamodzi ndi atumiki ake ndi anthu ake atakwera magaleta ndi mahatchi.”’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena