Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 2:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pamapeto pake Abineri anauza Yowabu kuti: “Bwanji anyamata athu anyamuke ndipo amenyane tione.” Poyankha, Yowabu anati: “Chabwino, zitero.”

  • 2 Mbiri 25:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Tsopano Amaziya mfumu ya Yuda anakambirana ndi anthu ena n’kutumiza uthenga kwa Yehoasi, mwana wa Yehoahazi mwana wa Yehu, mfumu ya Isiraeli,+ wakuti: “Bwera tidzamenyane.”+

  • Miyambo 13:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chifukwa cha kudzikuza, munthu amangoyambitsa mavuto,+ koma anthu amene amakhala pamodzi n’kumakambirana amakhala ndi nzeru.+

  • Miyambo 18:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Milomo ya munthu wopusa imalowa mu mkangano,+ ndipo pakamwa pake pamaitana zikwapu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena