Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye amadzutsa wonyozeka, kumuchotsa pafumbi.+

      Amachotsa osauka padzala,+

      Kuti awakhazike pakati pa anthu olemekezeka,+ ndipo amawapatsa mpando wachifumu waulemerero.+

      Pakuti michirikizo ya dziko lapansi ndi ya Yehova,+

      Ndipo anakhazika dziko lapansi pamichirikizo imeneyo.

  • Salimo 89:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pa nthawi imeneyo munalankhula ndi okhulupirika anu mwa masomphenya,+

      Ndipo munati:

      “Ndapereka thandizo kwa wamphamvu.+

      Ndakweza wosankhidwa mwapadera pakati pa anthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena