-
1 Mbiri 28:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Tsopano mwaima pamaso pa Aisiraeli onse, amene ndi mpingo wa Yehova,+ ndiponso Mulungu wathu akumva zimenezi.+ Choncho samalani ndi kutsatira malamulo onse a Yehova Mulungu wanu, kuti dziko labwinoli+ likhale lanu ndi kuti mudzasiyire ana anu obwera pambuyo panu monga cholowa chawo mpaka kalekale.
-