2 Samueli 5:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Davide anali ndi zaka 30 pamene anakhala mfumu. Iye analamulira monga mfumu kwa zaka 40.+ 1 Mafumu 2:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Davide analamulira Isiraeli zaka 40.+ Ku Heburoni+ analamulira zaka 7,+ ndipo ku Yerusalemu analamulira zaka 33.+
11 Davide analamulira Isiraeli zaka 40.+ Ku Heburoni+ analamulira zaka 7,+ ndipo ku Yerusalemu analamulira zaka 33.+