Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 21:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Iwo anapitiriza kunena kuti: “Ndani mwa mafuko a Isiraeli amene sanabwere kwa Yehova ku Mizipa?”+ Pamenepo anaona kuti ku msasawo sikunabwere aliyense wochokera ku Yabesi-giliyadi+ kudzagwirizana ndi mpingowo.

  • 1 Samueli 11:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiyeno Nahasi Muamoni+ anapita kukamanga msasa kuti amenyane ndi mzinda wa Yabesi+ ku Giliyadi. Zitatero, amuna onse a ku Yabesi anauza Nahasi kuti: “Chita nafe pangano kuti tizikutumikira.”+

  • 1 Samueli 31:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Nthawi yomweyo, amuna olimba mtima ananyamuka ndi kuyenda usiku wonse kukachotsa mtembo wa Sauli ndi mitembo ya ana ake pakhoma la ku Beti-sani. Kenako anabwerera ku Yabesi ndi kutentha mitemboyo kumeneko.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena