Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Kunena za Gadi, gulu la achifwamba lidzamuukira, koma iye adzawathira nkhondo, ndipo achifwambawo pothawa iye adzawakantha koopsa.+

  • Deuteronomo 33:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndipo kwa Gadi anati:+

      “Wodala ndi iye wofutukula malire a dera la Gadi.+

      Iye adzakhala ngati mkango,+

      Ndipo adzakhadzula dzanja, adzang’amba mutu paliwombo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena