Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Idzaika anthu ena kukhala atsogoleri a magulu a anthu 1,000+ ndi atsogoleri a magulu a anthu 50.+ Ena azidzalima minda yake+ ndi kukolola mbewu zake,+ ndiponso ena azidzapanga zida zake zankhondo+ ndi zida zogwiritsa ntchito pamagaleta ake.+

  • 1 Samueli 22:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Iye anauza atumiki ake amene anali atamuzungulirawo kuti: “Tamverani inu Abenjamini. Kodi nayenso mwana wa Jese+ adzakupatsani minda ya mpesa ndi minda ya mbewu zina?+ Kodi nonsenu adzakuikani kukhala atsogoleri a magulu a anthu 1,000+ ndi atsogoleri a magulu a anthu 100?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena