Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 16:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 M’patseni Yehova ulemerero wa dzina lake,+

      Tengani mphatso n’kubwera nayo pamaso pake.+

      Gwadirani Yehova mutavala zovala zokongola ndi zopatulika.+

  • Salimo 29:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 M’patseni Yehova ulemerero woyenera dzina lake.+

      Weramirani Yehova mutavala zovala zopatulika zokongola.+

  • Salimo 96:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Gwadirani Yehova mutavala zovala zokongola ndi zopatulika.+

      Njenjemerani ndi mantha aakulu* pamaso pake, inu anthu nonse okhala padziko lapansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena