Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 8:61
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 61 Mutumikire Yehova Mulungu wathu ndi mtima wathunthu+ mwa kuyenda motsatira malangizo ake ndi kusunga malamulo ake, monga mmene mukuchitira lero.”

  • 1 Mafumu 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pamene iye anali kukalamba,+ akazi ake anali atapotoza+ mtima wake moti iye anali kutsatira milungu ina.+ Sanatumikire Yehova Mulungu wake ndi mtima wathunthu+ monga mmene anachitira Davide bambo ake.

  • 2 Mafumu 14:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Iye anapitiriza kuchita zolungama pamaso pa Yehova,+ koma osati ngati Davide kholo lake.+ Anachita mogwirizana ndi zonse zimene Yehoasi bambo ake anachita.+

  • Salimo 78:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Mtima wawo sunali wokhulupirika kwa iye.+

      Ndipo iwo sanakhulupirike ku pangano lake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena