Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 9:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ku Yezereeliko,+ mlonda+ amene anaimirira pansanja+ anaona gulu lankhondo la Yehu likubwera mwaliwiro. Nthawi yomweyo mlondayo anati: “Ndikuona gulu la amuna likubwera mwaliwiro.” Pamenepo Yehoramu anati: “Uza munthu wokwera hatchi kuti apite kukakumana nawo. Akawafunse kuti, ‘Kodi mukubwerera zamtendere?’”+

  • 2 Mbiri 26:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iye anamanganso nsanja+ m’chipululu ndipo anakumba zitsime zambiri (popeza anakhala ndi ziweto zambiri). Anapanganso zomwezo ku Sefela+ ndi kudera lokwererapo. Kumapiri ndi ku Karimeli kunali alimi ndi anthu osamalira minda ya mpesa popeza iye ankakonda ulimi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena