Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 16:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mfumuyo itabwerako ku Damasiko, inaliona guwa lansembelo, ndipo inayamba kupita kuguwalo+ kukapereka nsembe.+

  • 2 Mafumu 16:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Paguwa lansembelo, mfumuyo inapitiriza kuwotchapo+ nsembe yopsereza+ ndi nsembe yambewu,+ ndi kuthirapo nsembe yachakumwa+ ndiponso kuwazapo magazi a nsembe zake zachiyanjano.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena