Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 18:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Kodi pali mulungu wa mitundu ina amene wakwanitsa kupulumutsa+ mtundu wake m’manja mwa mfumu ya Asuri?+

  • 2 Mafumu 19:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Atentha milungu yawo pamoto, chifukwa sinali milungu,+ koma ntchito ya manja a anthu,+ mitengo ndi miyala, n’chifukwa chake anaiwononga.

  • Salimo 115:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Amene amawapanga adzafanana nawo.+

      Onse amene amawakhulupirira adzakhala ngati mafanowo.+

  • Yesaya 44:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Anthu inu musachite mantha ndipo musathedwe nzeru.+ Kodi sindinachititse aliyense wa inu kuti amve kuyambira nthawi imeneyo? Kodi sindinakuuzeni zimenezi?+ Inu ndinu mboni zanga.+ Kodi palinso Mulungu kupatulapo ine?+ Ayi, palibe Thanthwe.+ Sindikudziwapo aliyense.’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena