Deuteronomo 28:50 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 50 mtundu wa nkhope yoopsa+ umene sudzaikira kumbuyo munthu wachikulire kapena kukondera mnyamata.+ Maliro 2:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Anyamata ndi amuna okalamba+ agona pansi m’misewu.+Anamwali anga ndi anyamata anga aphedwa ndi lupanga.+Mwapha anthu pa tsiku la mkwiyo+ wanu. Onsewo mwawaphadi+ mopanda chisoni.+
21 Anyamata ndi amuna okalamba+ agona pansi m’misewu.+Anamwali anga ndi anyamata anga aphedwa ndi lupanga.+Mwapha anthu pa tsiku la mkwiyo+ wanu. Onsewo mwawaphadi+ mopanda chisoni.+