Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 9:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pakuti imfa yatilowera m’nyumba kudzera m’mawindo. Yalowa munsanja zathu zokhalamo kuti mumsewu musapezeke mwana aliyense ndiponso kuti anyamata asapezeke m’mabwalo a mzinda.’+

  • Yeremiya 18:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chotero ana awo muwakhaulitse ndi njala yaikulu,+ ndipo aphedwe ndi lupanga.+ Akazi awo akhale amasiye ndipo ana a akaziwo afe.+ Amuna awo afe ndi mliri woopsa ndipo anyamata awo aphedwe ndi lupanga pa nkhondo.+

  • Maliro 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yehova wandichotsera anthu anga onse amphamvu+ ndi kuwakankhira pambali.

      Wandiitanitsira msonkhano kuti athyolethyole anyamata anga.+

      Yehova wapondaponda moponderamo mphesa+ mwa namwali, mwana wamkazi wa Yuda.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena