Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 109:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ana ake azingoyendayenda ndithu,+

      Ndipo azipemphapempha.

      Azichoka m’mabwinja mmene akukhala, n’kupita kukafunafuna chakudya.+

  • Yeremiya 11:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Yehova wa makamu wanena kuti: “Tsopano ndikuwapatsa chilango. Anyamata adzafa ndi lupanga.+ Ana awo aamuna ndi aakazi adzafa ndi njala yaikulu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena