Genesis 36:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 36 Mbiri ya Esau, kapena kuti Edomu,+ ili motere: 1 Mafumu 9:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Panali zombo zimene Mfumu Solomo inapanga ku Ezioni-geberi,+ pafupi ndi Eloti,+ pagombe la Nyanja Yofiira m’dziko la Edomu.+
26 Panali zombo zimene Mfumu Solomo inapanga ku Ezioni-geberi,+ pafupi ndi Eloti,+ pagombe la Nyanja Yofiira m’dziko la Edomu.+