Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 33:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Kenako ananyamuka ku Abirona n’kukamanga msasa ku Ezioni-geberi.+

  • Deuteronomo 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Chotero tinalambalala abale athu, ana a Esau,+ amene akukhala m’Seiri, ndipo sitinayende njira ya Araba,+ Elati ndi Ezioni-geberi.+

      “Kenako tinatembenuka ndi kudutsa njira ya m’chipululu cha Mowabu.+

  • 1 Mafumu 22:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Yehosafati anapanga zombo za ku Tarisi+ kuti zizipita ku Ofiri kukatenga golide, koma sizinapite chifukwa zinasweka ku Ezioni-geberi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena