1 Mafumu 9:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Anamanganso mizinda yake yonse yosungirako zinthu,+ mizinda yosungirako magaleta,+ mizinda ya amuna okwera pamahatchi, ndiponso zilizonse zimene iye anakonda+ kumanga ku Yerusalemu, ku Lebanoni, ndi m’dziko lonse limene ankalamulira. 2 Mbiri 8:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Kenako anamanganso mzinda wa Tadimori m’chipululu ndi mizinda yonse yosungiramo zinthu+ imene anamanga ku Hamati.+
19 Anamanganso mizinda yake yonse yosungirako zinthu,+ mizinda yosungirako magaleta,+ mizinda ya amuna okwera pamahatchi, ndiponso zilizonse zimene iye anakonda+ kumanga ku Yerusalemu, ku Lebanoni, ndi m’dziko lonse limene ankalamulira.
4 Kenako anamanganso mzinda wa Tadimori m’chipululu ndi mizinda yonse yosungiramo zinthu+ imene anamanga ku Hamati.+