12 Pamenepo iye anandiuza kuti: “Iwe Danieli, usaope,+ pakuti kuyambira tsiku loyamba pamene unatsegula mtima wako kuti umvetse tanthauzo la zinthu zimenezi,+ ndiponso pamene unadzichepetsa pamaso pa Mulungu wako,+ mawu ako akhala akumveka ndipo ine ndabwera chifukwa cha mawu akowo.+