Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 33:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndipo ndidziwa bwanji kuti mwandikomera mtima, ineyo ndi anthu anu? Si mwa kuyenda nafe kodi?+ Pajatu ine ndi anthu anu mwatisiyanitsa ndi anthu ena onse amene ali padziko lapansi.”+

  • Ezara 6:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiyeno ana a Isiraeli amene anabwera kuchokera ku ukapolo anadya+ nyamayo. Komanso aliyense amene anadzilekanitsa ku zonyansa+ za anthu a mitundu ina ya m’dzikolo n’kubwera kwa iwo ndi kufunafuna Yehova Mulungu wa Isiraeli, anadya nawo.+

  • Nehemiya 9:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Pamenepo mbewu ya Isiraeli inadzipatula+ kwa anthu onse osakhala Aisiraeli.+ Atatero anaimirira ndi kuulula+ machimo awo+ ndi zolakwa za makolo awo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena