16 Malirewo anatsetserekera kuphiri loyang’anizana ndi chigwa cha mwana wa Hinomu,+ limene linathera kumpoto kwa chigwa cha Arefai.+ Kenako anatsetserekera kuchigwa cha Hinomu kum’mwera kwa malo otsetsereka otchedwa Yebusi,+ n’kutsetserekabe mpaka ku Eni-rogeli.+