Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 15:63
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 63 Ana a Yuda analephera kupitikitsa+ Ayebusi+ omwe anali kukhala ku Yerusalemu,+ moti Ayebusi akukhalabe limodzi ndi ana a Yuda ku Yerusalemu mpaka lero.

  • Oweruza 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno ana a Yuda anapitiriza kumenyana ndi mzinda wa Yerusalemu+ n’kuulanda. Anapha anthu okhala mmenemo ndi lupanga, ndipo mzindawo anautentha ndi moto.

  • Oweruza 19:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma mwamunayo sanavomere kuti agone, ndipo ananyamuka ndi kuyamba ulendo wake. Iye anayenda mpaka kukafika pafupi ndi Yebusi,+ amene ndi Yerusalemu.+ Pa ulendowu, anali ndi abulu awiri amphongo aja, okhala ndi zishalo, ndipo analinso ndi mdzakazi wake ndi mtumiki wake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena