Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 10:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Panalinso Alevi awa amene anatsimikizira panganoli: Yesuwa,+ mwana wamwamuna wa Azaniya, Binui wochokera pakati pa ana a Henadadi,+ Kadimiyeli,

  • Nehemiya 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno panali Alevi awa: Yesuwa,+ Binui,+ Kadimiyeli,+ Serebiya, Yuda ndi Mataniya.+ Mataniya ndi abale akewa anali oyang’anira oimba nyimbo zoyamika Mulungu.

  • Nehemiya 12:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Atsogoleri a Alevi anali Hasabiya, Serebiya+ ndi Yesuwa mwana wa Kadimiyeli.+ Ndipo abale awo anaima moyang’anizana nawo kuti azitamanda ndi kuyamika Mulungu mogwirizana ndi lamulo+ la Davide, munthu wa Mulungu woona. Gulu lililonse la alonda linaima moyandikana ndi gulu lina la alonda.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena