Nehemiya 3:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Hananiya mwana wamwamuna wa Selemiya ndi Hanuni mwana wamwamuna wa 6 wa Zalafi, anakonzanso chigawo china cha mpanda. Kenako Mesulamu+ mwana wamwamuna wa Berekiya, anakonza mpandawo kutsogolo kwa nyumba* yake kuchokera pamene winayo analekezera.+ Nehemiya 6:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Pakuti anthu ambiri mu Yuda anamulumbirira kukhala naye mwamtendere chifukwa anali mkamwini wa Sekaniya, mwana wamwamuna wa Ara.+ Ndipo Yehohanani mwana wamwamuna wa Tobia, anakwatira mwana wamkazi wa Mesulamu,+ mwana wamwamuna wa Berekiya.
30 Hananiya mwana wamwamuna wa Selemiya ndi Hanuni mwana wamwamuna wa 6 wa Zalafi, anakonzanso chigawo china cha mpanda. Kenako Mesulamu+ mwana wamwamuna wa Berekiya, anakonza mpandawo kutsogolo kwa nyumba* yake kuchokera pamene winayo analekezera.+
18 Pakuti anthu ambiri mu Yuda anamulumbirira kukhala naye mwamtendere chifukwa anali mkamwini wa Sekaniya, mwana wamwamuna wa Ara.+ Ndipo Yehohanani mwana wamwamuna wa Tobia, anakwatira mwana wamkazi wa Mesulamu,+ mwana wamwamuna wa Berekiya.