Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 39:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Anaika belu ndi khangaza,* belu ndi khangaza, kuzungulira mpendero wa m’munsi mwa malaya odula manja.+ Malayawo ndi oti azivala potumikira, monga mmene Yehova analamulira Mose.

  • Numeri 8:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Iye azingothandizira abale ake m’chihema chokumanako pochita utumiki wawo, koma asatumikire. Umu ndi mmene uzichitira ndi Alevi malinga ndi ntchito zawo.”+

  • Deuteronomo 18:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pakuti iye ndi amene Yehova Mulungu wako wam’sankha pakati pa mafuko anu onse, kuti iye pamodzi ndi ana ake aimirire ndi kutumikira m’dzina la Yehova nthawi zonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena