Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 13:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndiyeno ndinazindikira kuti magawo+ a Alevi sanali kuperekedwa kwa iwo, moti aliyense wa Aleviwo ndi oimba amene anali kutumikira anathawa ndipo anapita kumunda wake.+

  • Nehemiya 13:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Zitatero ndinayamba kuimba mlandu+ atsogoleriwo+ ndi kuwafunsa kuti: “N’chifukwa chiyani nyumba ya Mulungu woona yasiyidwa chonchi?”+ Pamenepo ndinawasonkhanitsa pamodzi ndipo ndinawaika pamalo awo ogwirira ntchito.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena