Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 9:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Panalinso Bakabakara, Heresi, Galali, ndi Mataniya+ mwana wa Mika.+ Mika anali mwana wa Zikiri,+ ndipo Zikiri anali mwana wa Asafu.+

  • Nehemiya 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno panali Alevi awa: Yesuwa,+ Binui,+ Kadimiyeli,+ Serebiya, Yuda ndi Mataniya.+ Mataniya ndi abale akewa anali oyang’anira oimba nyimbo zoyamika Mulungu.

  • Nehemiya 13:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno ndinaika Selemiya wansembe, Zadoki wokopera Malemba ndi Pedaya mmodzi mwa Alevi, kuti akhale oyang’anira malo osungira zinthu. Amenewa anali kuyang’anira Hanani mwana wa Zakuri amene anali mwana wa Mataniya,+ pakuti anthu anali kuwaona kuti ndi okhulupirika.+ Iwowa anapatsidwa udindo wogawa+ zinthu kwa abale awo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena