Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 2:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 M’masiku amenewo, pamene Moredekai anali kukhala pansi kuchipata cha mfumu, Bigitana ndi Teresi, nduna ziwiri za panyumba ya mfumu, amenenso anali alonda a pakhomo, anakwiya ndipo anafuna kupha+ Mfumu Ahasiwero.

  • Esitere 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno atumiki a mfumu amene anali kuchipatako anayamba kufunsa Moredekai kuti: “N’chifukwa chiyani ukunyalanyaza lamulo la mfumu?”+

  • Esitere 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Nthawi yomweyo mfumu inauza Hamani kuti: “Fulumira, tenga chovala ndi hatchi monga mmene wanenera, ndipo ukachitire zimenezi Moredekai, Myuda, amene ali kuchipata. Uonetsetse kuti zonse zimene wanenazi zakwaniritsidwa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena