-
Esitere 2:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Ndiyeno inu mfumu musankhe anthu m’zigawo zonse+ za ufumu wanu. Anthuwo asonkhanitse pamodzi atsikana onse, anamwali okongola, kunyumba ya mfumu yokhala ndi mpanda wolimba kwambiri ya ku Susani,+ m’nyumba ya akazi imene Hegai+ akuyang’anira. Iye ndi munthu wofulidwa wa mfumu+ woyang’anira akazi, amenenso ndi mkulu woyang’anira nyumba ya akazi. Ndipo kumeneko atsikanawo azikawapaka mafuta okongoletsa.
-