Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 2:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Madzulo mtsikanayo anali kubwera kwa mfumu, ndipo m’mawa anali kubwerera kunyumba yachiwiri ya akazi, imene Sasigazi anali kuyang’anira. Sasigazi anali munthu wofulidwa wa mfumu,+ mkulu woyang’anira akazi. Mtsikanayo sanalinso kubwera kwa mfumu pokhapokha ngati mfumuyo yakondwera naye ndipo yamuitanitsa mwa kum’tchula dzina.+

  • Esitere 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno atsikana otumikira Esitere ndi amuna ofulidwa+ amene anali kumuyang’anira anayamba kubwera kudzamuuza zimenezi. Ndipo mfumukaziyo inamva chisoni kwambiri, choncho inatumiza zovala kuti Moredekai akavule zigudulizo ndi kuvala zovalazo, koma Moredekai sanalole.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena