-
Esitere 2:14Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 Madzulo mtsikanayo anali kubwera kwa mfumu, ndipo m’mawa anali kubwerera kunyumba yachiwiri ya akazi, imene Sasigazi anali kuyang’anira. Sasigazi anali munthu wofulidwa wa mfumu,+ mkulu woyang’anira akazi. Mtsikanayo sanalinso kubwera kwa mfumu pokhapokha ngati mfumuyo yakondwera naye ndipo yamuitanitsa mwa kum’tchula dzina.+
-