Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 2:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndiyeno nthawi itakwana yoti Esitere akaonekere kwa mfumu, sanapemphe kalikonse+ kupatulapo zimene Hegai+ anatchula. Iye anali munthu wofulidwa wa mfumu woyang’anira akazi, amenenso anali mkulu woyang’anira nyumba ya akazi. Esitere anali mwana wa Abihaili, m’bale wa bambo ake a Moredekai, amene Moredekai anamutenga ngati mwana wake+ (pa nthawi imeneyi Esitere anali kukondedwa ndi aliyense womuona).+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena