Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Dzanja lanu lamanja, inu Yehova, likusonyeza kupambana kwa mphamvu zake.+

      Dzanja lanu lamanja, inu Yehova, limaphwanya mdani.+

  • Salimo 89:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mkono wamphamvu ndi wanu,+

      Dzanja lanu ndi lamphamvu,+

      Dzanja lanu lamanja ndi lokwezeka.+

  • 1 Akorinto 10:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Kapena “kodi tikufuna kuputa nsanje+ ya Yehova”? Kodi mphamvu zathu zingafanane ndi zake?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena