Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 17:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Sonyezani kukoma mtima kosatha mwa kuchita zodabwitsa,+ inu Mpulumutsi wa anthu othawira kwa inu,

      Amene akuthawa anthu ogalukira dzanja lanu lamanja.+

  • Salimo 60:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Kuti okondedwa anu apulumutsidwe,+

      Tipulumutseni ndi dzanja lanu lamanja ndi kutiyankha.+

  • Salimo 89:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mkono wamphamvu ndi wanu,+

      Dzanja lanu ndi lamphamvu,+

      Dzanja lanu lamanja ndi lokwezeka.+

  • Salimo 118:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 M’mahema+ a olungama+

      Mumamveka mfuu yachisangalalo ndipo muli chipulumutso.+

      Dzanja lamanja la Yehova limachita zamphamvu.+

  • 1 Petulo 5:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Choncho dzichepetseni pansi pa dzanja lamphamvu la Mulungu, kuti adzakukwezeni m’nthawi yake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena