Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 18:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Inu mudzandipatsa chishango chanu cha chipulumutso,+

      Dzanja lanu lamanja lidzandichirikiza,+

      Ndipo kudzichepetsa kwanu n’kumene kudzandikweza.+

  • Salimo 21:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Dzanja lanu lidzapeza adani anu onse.+

      Dzanja lanu lamanja lidzapeza odana nanu.

  • Salimo 118:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 M’mahema+ a olungama+

      Mumamveka mfuu yachisangalalo ndipo muli chipulumutso.+

      Dzanja lamanja la Yehova limachita zamphamvu.+

  • Yesaya 41:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Usachite mantha, pakuti ndili nawe.+ Usayang’ane uku ndi uku mwamantha, pakuti ine ndine Mulungu wako.+ Ndikulimbitsa.+ Ndithu ndikuthandiza.+ Ndikugwira mwamphamvu ndi dzanja langa lamanja+ lachilungamo.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena