Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 9:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pamenepo udzachuluka ndi kugwa ngati fumbi padziko lonse la Iguputo. Ukatero udzayambitsa zithupsa zimene zizidzaphulika+ pa anthu ndi nyama zomwe, m’dziko lonse la Iguputo.”

  • Levitiko 13:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 “Ngati pakhungu la munthu pali chithupsa,+ ndipo kenako chapola,

  • Yobu 30:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Khungu langa linakhala lakuda+ ndipo linayoyoka pathupi panga.

      Mafupa anga anatentha chifukwa chouma.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena