Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 19:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ineyo ndikudziwa bwino kuti wondiwombola+ ali moyo,

      Ndipo adzabwera pambuyo panga n’kuimirira+ pafumbi.

  • Salimo 49:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Palibe ngakhale mmodzi wa iwo amene angathe kuwombola m’bale wake,+

      Kapena kumuperekera dipo* kwa Mulungu,

  • Mateyu 20:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Mofanana ndi zimenezi, Mwana wa munthu sanabwere kudzatumikiridwa, koma kudzatumikira+ ndi kudzapereka moyo wake dipo* kuwombola anthu ambiri.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena