Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Pa nthawi imeneyo tinalanda dziko m’manja mwa mafumu awiri amenewo a Aamori+ amene anali kukhala m’dera la Yorodano, kuyambira m’chigwa* cha Arinoni+ mpaka kuphiri la Herimoni.+

  • Deuteronomo 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tinalanda mizinda yonse ya kudera lokwererapo, m’Giliyadi monse, m’Basana monse, mpaka ku Saleka+ ndi ku Edirei,+ mizinda ya m’dera la ufumu wa Ogi ku Basana.

  • Salimo 42:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Inu Mulungu wanga, ine ndataya mtima.+

      N’chifukwa chake ndakumbukira inu,+

      Pamene ndili m’dziko la Yorodano ndi m’mapiri a Herimoni,+

      Pamene ndili m’phiri laling’ono.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena